BENGO NDI ABUSA AKE PA 4N

BENGO : Hello abusa, muli pa Airtel Money ngat?

ABUSA : Kumwamba kulemekezeke masiku onse, eya atsogoleri ndili pa airtel money angakhaleso pa Mpamba.

BENGO : Apa muli bize ngati?

ABUSA : Ai atsogoleri, Apa ndangomaliza kumene kupempherera nkhosa zanga, banja lanu komanso utumiki wa mpingo onse.

BENGO : Ok, ndimafuna mundithandize kusintha pin code, paja amatani?

ABUSA : Pamsana panu atsogoleri

BENGO : Inunso pamsana panu abusa

Werengani Nkhani za Bengo zinanso




Back Home Up